-
Danieli 5:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Pa nthawi imeneyo anabweretsa ziwiya zagolide zimene anazitenga m’kachisi, m’nyumba ya Mulungu ku Yerusalemu. Kenako mfumuyo, nduna zake, adzakazi ake ndi akazi ake ena apambali anayamba kumwera m’ziwiyazo.
-