Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako, Yehova Mulungu anaumba munthu kuchokera kufumbi lapansi,+ ndipo anauzira mpweya wa moyo+ m’mphuno mwake, munthuyo n’kukhala wamoyo.+

  • Deuteronomo 4:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 “Tafunsani tsopano, za masiku akale+ inu musanakhalepo, kuchokera pa tsiku limene Mulungu analenga munthu padziko lapansi,+ ndiponso kuchokera kumalekezero ena a thambo kukafika kumalekezero ena a thambo, Kodi chinthu chachikulu ngati chimenechi chinayamba chachitikapo, kapena kodi chinthu ngati chimenechi chinayamba chamvekapo?+

  • Yesaya 57:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pakuti ine sindidzatsutsana nanu mpaka kalekale, ndiponso sindidzakhala wokwiya mpaka kalekale.+ Popeza chifukwa cha ine, mzimu wa munthu ukhoza kufooka,+ ngakhalenso zinthu zopuma zimene ineyo ndinapanga.+

  • Yeremiya 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ‘Ine ndinapanga dziko lapansi,+ anthu+ ndi nyama+ zapadziko lapansi pogwiritsa ntchito mphamvu zanga zazikulu+ ndiponso dzanja langa lotambasula.+ Ndipo dzikoli ndalipereka kwa amene ndikufuna.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena