Yoswa 24:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Mukasiya Yehova+ n’kuyamba kutumikira milungu yachilendo,+ iyenso adzakutembenukirani ndithu, n’kukuchitirani zoipa ndi kukufafanizani, pambuyo pokuchitirani zabwino.”+ 2 Mafumu 22:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 chifukwa chakuti andisiya n’kumakafukiza nsembe yautsi kwa milungu ina+ kuti andikwiyitse ndi ntchito zonse za manja awo.+ Choncho mkwiyo wanga wayakira malo ano ndipo suzimitsidwa.’”’+ 2 Mbiri 7:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma inuyo mukadzabwerera+ n’kusiya kutsatira malamulo anga+ amene ndakupatsani, komanso mukadzapita kukatumikira milungu ina+ ndi kuigwadira,+ Yeremiya 17:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Inu Yehova, chiyembekezo cha Isiraeli,+ onse amene akukusiyani adzachita manyazi.+ Mayina a anthu onse okupandukirani+ adzalembedwa pafumbi chifukwa asiya Yehova magwero a madzi amoyo.+
20 Mukasiya Yehova+ n’kuyamba kutumikira milungu yachilendo,+ iyenso adzakutembenukirani ndithu, n’kukuchitirani zoipa ndi kukufafanizani, pambuyo pokuchitirani zabwino.”+
17 chifukwa chakuti andisiya n’kumakafukiza nsembe yautsi kwa milungu ina+ kuti andikwiyitse ndi ntchito zonse za manja awo.+ Choncho mkwiyo wanga wayakira malo ano ndipo suzimitsidwa.’”’+
19 Koma inuyo mukadzabwerera+ n’kusiya kutsatira malamulo anga+ amene ndakupatsani, komanso mukadzapita kukatumikira milungu ina+ ndi kuigwadira,+
13 Inu Yehova, chiyembekezo cha Isiraeli,+ onse amene akukusiyani adzachita manyazi.+ Mayina a anthu onse okupandukirani+ adzalembedwa pafumbi chifukwa asiya Yehova magwero a madzi amoyo.+