Yesaya 21:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Uwu ndi uthenga wokhudza Duma: Ndikumva winawake akundifunsa mofuula kuchokera ku Seiri+ kuti: “Mlonda, kodi usiku watsala wotalika bwanji? Mlonda, kodi usiku watsala wotalika bwanji?”+ Yeremiya 25:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Yehova anakutumizirani atumiki ake onse aneneri. Anali kudzuka m’mawa kwambiri ndi kuwatumiza, koma inu simunawamvere+ kapena kutchera khutu lanu kuti mumvetsere.+ Ezekieli 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 “Iwe mwana wa munthu, ine ndakuika kuti ukhale mlonda wa nyumba ya Isiraeli.+ Umve mawu ochokera pakamwa panga ndipo undichenjezere anthuwo.+ Habakuku 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ine ndidzaimabe+ pamalo a mlonda ndiponso pakhoma lachitetezo. Ndidzakhala tcheru+ kuti ndione uthenga umene iye adzalankhula kudzera mwa ine+ ndi zimene ndidzayankha pamene iye akundidzudzula.+
11 Uwu ndi uthenga wokhudza Duma: Ndikumva winawake akundifunsa mofuula kuchokera ku Seiri+ kuti: “Mlonda, kodi usiku watsala wotalika bwanji? Mlonda, kodi usiku watsala wotalika bwanji?”+
4 Yehova anakutumizirani atumiki ake onse aneneri. Anali kudzuka m’mawa kwambiri ndi kuwatumiza, koma inu simunawamvere+ kapena kutchera khutu lanu kuti mumvetsere.+
17 “Iwe mwana wa munthu, ine ndakuika kuti ukhale mlonda wa nyumba ya Isiraeli.+ Umve mawu ochokera pakamwa panga ndipo undichenjezere anthuwo.+
2 Ine ndidzaimabe+ pamalo a mlonda ndiponso pakhoma lachitetezo. Ndidzakhala tcheru+ kuti ndione uthenga umene iye adzalankhula kudzera mwa ine+ ndi zimene ndidzayankha pamene iye akundidzudzula.+