2 “Lankhula ndi ana a Isiraeli kuti abwerere ndi kumanga msasa pafupi ndi Pihahiroti, pakati pa Migidoli ndi nyanja, koma moyang’anizana ndi Baala-zefoni.+ Mumange msasa wanu pafupi ndi nyanja, patsogolo pa Baala-zefoni.
14 “Nenani zimenezi mu Iguputo amuna inu. Lengezani zimenezi ku Migidoli,+ ku Nofi+ ndi ku Tahapanesi.+ Nenani kuti, ‘Imani chilili. Konzekani.+ Pakuti lupanga lidzawononga chilichonse chokuzungulirani.+