Ekisodo 29:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 Choncho ndidzakhala pakati pa ana a Isiraeli, ndipo ndidzakhala Mulungu wawo.+ Salimo 68:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 N’chifukwa chiyani inu mapiri a nsonga zitalizitali mumayang’ana mwanjiruPhiri limene Mulungu wafuna kukhalamo?+Yehova adzakhala m’phiri limenelo mpaka muyaya.+ Salimo 132:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “Awa ndi malo anga okhalamo mpaka muyaya.+Ndidzakhala mmenemu, pakuti ndimafunitsitsa kukhala m’malo amenewa.+ Yoweli 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Pamenepo anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu,+ amene ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika.+ Yerusalemu adzakhala malo anga opatulika,+ ndipo alendo sadzadutsanso mmenemo.+ 2 Akorinto 6:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Ndipo pali kumvana kotani pakati pa kachisi wa Mulungu ndi mafano?+ Pakuti ifeyo ndife kachisi+ wa Mulungu wamoyo, monga ananenera Mulungu kuti: “Ndidzakhala pakati pawo+ ndi kuyenda pakati pawo. Ndidzakhala Mulungu wawo, ndipo iwo adzakhala anthu anga.”+
16 N’chifukwa chiyani inu mapiri a nsonga zitalizitali mumayang’ana mwanjiruPhiri limene Mulungu wafuna kukhalamo?+Yehova adzakhala m’phiri limenelo mpaka muyaya.+
14 “Awa ndi malo anga okhalamo mpaka muyaya.+Ndidzakhala mmenemu, pakuti ndimafunitsitsa kukhala m’malo amenewa.+
17 Pamenepo anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu,+ amene ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika.+ Yerusalemu adzakhala malo anga opatulika,+ ndipo alendo sadzadutsanso mmenemo.+
16 Ndipo pali kumvana kotani pakati pa kachisi wa Mulungu ndi mafano?+ Pakuti ifeyo ndife kachisi+ wa Mulungu wamoyo, monga ananenera Mulungu kuti: “Ndidzakhala pakati pawo+ ndi kuyenda pakati pawo. Ndidzakhala Mulungu wawo, ndipo iwo adzakhala anthu anga.”+