Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Choncho ndidzakhala pakati pa ana a Isiraeli, ndipo ndidzakhala Mulungu wawo.+

  • Salimo 68:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 N’chifukwa chiyani inu mapiri a nsonga zitalizitali mumayang’ana mwanjiru

      Phiri limene Mulungu wafuna kukhalamo?+

      Yehova adzakhala m’phiri limenelo mpaka muyaya.+

  • Salimo 132:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Awa ndi malo anga okhalamo mpaka muyaya.+

      Ndidzakhala mmenemu, pakuti ndimafunitsitsa kukhala m’malo amenewa.+

  • Yoweli 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu,+ amene ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika.+ Yerusalemu adzakhala malo anga opatulika,+ ndipo alendo sadzadutsanso mmenemo.+

  • 2 Akorinto 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndipo pali kumvana kotani pakati pa kachisi wa Mulungu ndi mafano?+ Pakuti ifeyo ndife kachisi+ wa Mulungu wamoyo, monga ananenera Mulungu kuti: “Ndidzakhala pakati pawo+ ndi kuyenda pakati pawo. Ndidzakhala Mulungu wawo, ndipo iwo adzakhala anthu anga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena