Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Choncho Yuda anapatukira kwa mkaziyo pambali pa msewu n’kumuuza kuti: “Ndikufuna ndigone nawe.”+ Anatero posadziwa kuti anali mpongozi wake.+ Koma mkaziyo anayankha kuti: “Mundipatsa chiyani kuti mugone nane?”+

  • Deuteronomo 23:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Usabweretse malipiro+ a hule kapena malipiro a galu*+ m’nyumba ya Yehova Mulungu wako kuti ukwaniritse lonjezo lililonse, chifukwa zonsezo ndi zonyansa kwa Yehova Mulungu wako.

  • Hoseya 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa+ ndi ya mkuyu+ imene iye anali kunena kuti: “Imeneyi ndi mphatso imene amuna ondikonda kwambiri anandipatsa.” Koma ine ndidzachititsa mitengoyo kukhala ngati nkhalango,+ ndipo zilombo zakutchire zidzaidya ndi kuiwononga.

  • Luka 15:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Koma atangofika mwana wanuyu,+ amene anadya chuma chanu ndi mahule,+ mwamuphera mwana wa ng’ombe wamphongo wonenepa bwino.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena