1 Samueli 28:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ngakhale kuti anali kufunsira kwa Yehova,+ Yehova sanamuyankhe+ kaya kudzera m’maloto,+ Urimu+ kapena kudzera mwa aneneri.+ Miyambo 15:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Nsembe ya anthu oipa imam’nyansa Yehova,+ koma pemphero la anthu owongoka mtima limam’sangalatsa.+ Miyambo 28:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Munthu amene amathawitsa khutu lake kuti asamve chilamulo,+ ngakhale pemphero lake limakhala lonyansa.+ Yesaya 1:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Mukatambasula manja anu,+ ndimakubisirani maso anga.+ Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+ ine sindimvetsera.+ Manja anu adzaza magazi amene mwakhetsa.+ Ezekieli 14:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “Iwe mwana wa munthu, amuna awa aika mitima yawo pamafano onyansa, ndipo aika pamaso pawo chinthu chopunthwitsa chimene chimawalakwitsa.+ Kodi ndiwayankhe iwo akamandifunsa?+ Mika 3:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Oona masomphenya+ adzachita manyazi+ ndipo olosera+ adzakhumudwa ndithu. Onsewa adzaphimba ndevu zawo zapamlomo+ chifukwa Mulungu sadzawayankha.’”+
6 Ngakhale kuti anali kufunsira kwa Yehova,+ Yehova sanamuyankhe+ kaya kudzera m’maloto,+ Urimu+ kapena kudzera mwa aneneri.+
9 Munthu amene amathawitsa khutu lake kuti asamve chilamulo,+ ngakhale pemphero lake limakhala lonyansa.+
15 Mukatambasula manja anu,+ ndimakubisirani maso anga.+ Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+ ine sindimvetsera.+ Manja anu adzaza magazi amene mwakhetsa.+
3 “Iwe mwana wa munthu, amuna awa aika mitima yawo pamafano onyansa, ndipo aika pamaso pawo chinthu chopunthwitsa chimene chimawalakwitsa.+ Kodi ndiwayankhe iwo akamandifunsa?+
7 Oona masomphenya+ adzachita manyazi+ ndipo olosera+ adzakhumudwa ndithu. Onsewa adzaphimba ndevu zawo zapamlomo+ chifukwa Mulungu sadzawayankha.’”+