-
Ezekieli 14:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Chotero lankhula nawo ndipo uwauze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Munthu aliyense wa nyumba ya Isiraeli amene waika mtima wake pamafano ake onyansa+ ndiponso amene waika pamaso pake chinthu chopunthwitsa chimene chimamulakwitsa n’kupita kwa mneneri, ine Yehova ndidzamuyankha malinga ndi kuchuluka kwa mafano ake onyansa.+
-