Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Zekariya 8:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Yehova wa makamu wanena kuti, ‘Kusala kudya kwa m’mwezi wachinayi,+ kusala kudya kwa m’mwezi wachisanu,+ kusala kudya kwa m’mwezi wa 7+ ndiponso kusala kudya kwa m’mwezi wa 10,+ kudzakhala kusala kudya kosangalatsa ndi kokondweretsa kwa nyumba ya Yuda. Komanso nthawi za kusala kudya zimenezi zidzakhala nyengo zabwino zazikondwerero.+ Choncho muzikonda choonadi ndi kulimbikitsa mtendere.’+

  • Machitidwe 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamene anali kutumikira+ Yehova ndi kusala kudya, mzimu woyera unati: “Mwa anthu onse, mundipatulire Baranaba ndi Saulo+ kuti agwire ntchito imene ndinawaitanira.”

  • Machitidwe 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pamenepo anasala kudya ndipo anapemphera, kenako anawaika manja+ ndi kuwalola kuti apite.

  • Machitidwe 14:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Komanso, anawaikira akulu+ mumpingo uliwonse, ndipo atapemphera ndi kusala kudya,+ anawapereka kwa Yehova+ yemwe anamukhulupirira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena