Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 27
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 27:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:32; 26:16; Lu 11:28

Deuteronomo 27:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:1; Yos 4:1

Deuteronomo 27:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 8:32
  • +Eks 24:12
  • +Le 20:24; Nu 13:27; 14:8; De 26:9; Yer 11:5; 32:22

Deuteronomo 27:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:29; Yos 8:30
  • +De 27:2

Deuteronomo 27:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:25; Yos 8:31

Deuteronomo 27:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 1:9

Deuteronomo 27:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 3:1
  • +Le 7:15
  • +De 12:7; 16:11

Deuteronomo 27:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:12
  • +Hab 2:2

Deuteronomo 27:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; De 26:18

Deuteronomo 27:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:6; 1Mf 2:3; Mt 19:17; 1Yo 5:3
  • +1Mf 8:61

Deuteronomo 27:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:29

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, ptsa. 30-31

    6/15/1996, tsa. 14

Deuteronomo 27:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Da 9:11
  • +Yos 8:33

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, ptsa. 30-31

    6/15/1996, tsa. 14

Deuteronomo 27:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 33:10; Ne 8:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1996, tsa. 14

Deuteronomo 27:15

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti “Ame!” m’Chiheberi.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:4; De 4:16; Yes 44:9
  • +Eks 34:17; Le 19:4; Nu 33:52
  • +De 7:25; 29:17
  • +Ho 13:2
  • +Nu 5:22; Ne 5:13

Deuteronomo 27:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:12; Le 19:3; De 21:18, 21; Miy 20:20; 30:17; Mt 15:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, ptsa. 30-31

Deuteronomo 27:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:14; Miy 22:28; 23:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1997, ptsa. 30-31

Deuteronomo 27:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:14

Deuteronomo 27:19

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwana wamwamuna wopanda bambo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 17:23; Mik 3:11
  • +De 16:20
  • +Eks 22:21
  • +Eks 22:22; De 10:18; 24:17; Mki 3:5; Yak 1:27

Deuteronomo 27:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:8; 2Sa 16:22; 1Ak 5:1

Deuteronomo 27:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:19; Le 18:23; 20:15

Deuteronomo 27:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:9; 20:17; 2Sa 13:14; Eze 22:11

Deuteronomo 27:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:17; 20:14

Deuteronomo 27:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:13; 21:12; Le 24:17; Nu 35:31

Deuteronomo 27:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:17; Eze 22:12; Mt 27:4; Mac 1:18

Deuteronomo 27:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:15; Sl 119:21; Yer 11:3; Aga 3:10

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 27:1De 11:32; 26:16; Lu 11:28
Deut. 27:2De 6:1; Yos 4:1
Deut. 27:3Yos 8:32
Deut. 27:3Eks 24:12
Deut. 27:3Le 20:24; Nu 13:27; 14:8; De 26:9; Yer 11:5; 32:22
Deut. 27:4De 11:29; Yos 8:30
Deut. 27:4De 27:2
Deut. 27:5Eks 20:25; Yos 8:31
Deut. 27:6Le 1:9
Deut. 27:7Le 3:1
Deut. 27:7Le 7:15
Deut. 27:7De 12:7; 16:11
Deut. 27:8Eks 24:12
Deut. 27:8Hab 2:2
Deut. 27:9Eks 19:5; De 26:18
Deut. 27:10Eks 20:6; 1Mf 2:3; Mt 19:17; 1Yo 5:3
Deut. 27:101Mf 8:61
Deut. 27:12De 11:29
Deut. 27:13Da 9:11
Deut. 27:13Yos 8:33
Deut. 27:14De 33:10; Ne 8:7
Deut. 27:15Eks 20:4; De 4:16; Yes 44:9
Deut. 27:15Eks 34:17; Le 19:4; Nu 33:52
Deut. 27:15De 7:25; 29:17
Deut. 27:15Ho 13:2
Deut. 27:15Nu 5:22; Ne 5:13
Deut. 27:16Eks 20:12; Le 19:3; De 21:18, 21; Miy 20:20; 30:17; Mt 15:4
Deut. 27:17De 19:14; Miy 22:28; 23:10
Deut. 27:18Le 19:14
Deut. 27:19Miy 17:23; Mik 3:11
Deut. 27:19De 16:20
Deut. 27:19Eks 22:21
Deut. 27:19Eks 22:22; De 10:18; 24:17; Mki 3:5; Yak 1:27
Deut. 27:20Le 18:8; 2Sa 16:22; 1Ak 5:1
Deut. 27:21Eks 22:19; Le 18:23; 20:15
Deut. 27:22Le 18:9; 20:17; 2Sa 13:14; Eze 22:11
Deut. 27:23Le 18:17; 20:14
Deut. 27:24Eks 20:13; 21:12; Le 24:17; Nu 35:31
Deut. 27:25De 10:17; Eze 22:12; Mt 27:4; Mac 1:18
Deut. 27:26De 28:15; Sl 119:21; Yer 11:3; Aga 3:10
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 27:1-26

Deuteronomo

27 Mose pamodzi ndi akulu a Isiraeli anapitiriza kuuza anthuwo kuti: “Muzisunga lamulo lililonse limene ndikukupatsani lero.+ 2 Mukawoloka Yorodano+ ndi kulowa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, muimike miyala ikuluikulu ndi kuipaka utoto woyera. 3 Ndiyeno mukawoloka,+ mulembe pamiyalapo mawu onse a chilamulochi+ kuti mulowe m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, dziko loyenda mkaka ndi uchi, malinga ndi zimene Yehova Mulungu wa makolo anu wakuuzani.+ 4 Choncho mukawoloka Yorodano, muimike miyala imeneyi paphiri la Ebala,+ monga mmene ndakulamulirani lero, ndipo muipake utoto woyera.+ 5 Mumangirenso Yehova Mulungu wanu guwa lansembe kumeneko, guwa lansembe lamiyala. Musaseme miyalayo ndi chipangizo chilichonse chachitsulo.+ 6 Muzigwiritsa ntchito miyala yathunthu pomangira Yehova Mulungu wanu guwa lansembe, ndipo muzipereka nsembe zopsereza kwa Yehova Mulungu wanu paguwalo.+ 7 Muzipereka nsembe zachiyanjano+ ndi kuzidyera pamenepo,+ ndipo muzikondwera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.+ 8 Mulembe mawu onse a chilamulochi pamiyalayo,+ muwalembe moonekera bwino.”+

9 Kenako Mose ndi ansembe achilevi analankhula ndi Aisiraeli onse kuti: “Aisiraeli inu, khalani chete ndi kumvetsera. Lero mwakhala anthu a Yehova Mulungu wanu.+ 10 Choncho muzimvera mawu a Yehova Mulungu wanu ndi kusunga malamulo+ ndi malangizo ake,+ amene ndikukupatsani lero.”

11 Tsiku limenelo Mose anapitiriza kulankhula ndi anthuwo kuti: 12 “Amene adzaimirira ndi kudalitsa anthu paphiri la Gerizimu+ mukawoloka Yorodano ndi awa: Simiyoni, Levi, Yuda, Isakara, Yosefe ndi Benjamini. 13 Amene adzaimirira kuti avomere pamene matemberero+ akutchulidwa paphiri la Ebala+ ndi awa: Rubeni, Gadi, Aseri, Zebuloni, Dani ndi Nafitali. 14 Pamenepo Alevi azinena mawu awa mokweza kuuza mwamuna aliyense wa Isiraeli+ kuti:

15 “‘Wotembereredwa ndi munthu aliyense wopanga chifaniziro chosema+ kapena chifaniziro chopangidwa ndi chitsulo chosungunula+ ndi kuchibisa. Chifanizirocho ndi chinthu chonyansa kwa Yehova,+ Mulungu wopanga manja a mmisiri wa matabwa ndi zitsulo.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)*+

16 “‘Wotembereredwa ndi munthu wonyoza bambo ake kapena mayi ake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

17 “‘Wotembereredwa ndi munthu wosuntha chizindikiro cha malire a mnzake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

18 “‘Wotembereredwa ndi munthu wosocheretsa wakhungu.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

19 “‘Wotembereredwa ndi munthu wopotoza+ chiweruzo+ cha mlendo wokhala pakati panu,+ mwana wamasiye* ndi mkazi wamasiye.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

20 “‘Wotembereredwa ndi munthu wogona ndi mkazi wa bambo ake, chifukwa wavula bambo akewo.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

21 “‘Wotembereredwa ndi munthu wogona nyama iliyonse.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

22 “‘Wotembereredwa ndi munthu wogona ndi mlongo wake, mwana wamkazi wa bambo ake kapena mwana wamkazi wa mayi ake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

23 “‘Wotembereredwa ndi mwamuna wogona ndi apongozi ake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

24 “‘Wotembereredwa ndi munthu wobisalira mnzake ndi kumupha.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

25 “‘Wotembereredwa ndi munthu wolandira chiphuphu kuti akanthe ndi kupheratu munthu, kuti akhetse magazi a munthu wosachimwa.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

26 “‘Wotembereredwa ndi munthu amene sadzatsatira mawu a m’chilamulo ichi ndipo sadzawagwiritsa ntchito.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena