Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ubweretse Aroni ndi ana ake pakhomo la chihema chokumanako,+ ndipo uwasambitse* ndi madzi.+

  • Ekisodo 29:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako utenge mafuta odzozera+ nʼkuwathira pamutu pake kuti akhale wodzozedwa.+

  • Ekisodo 30:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kenako udzoze Aroni+ ndi ana ake+ ndipo uwayeretse kuti atumikire monga ansembe anga.+

  • Ekisodo 40:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ukatero udzaveke Aroni zovala zopatulika+ kenako nʼkumudzoza+ komanso kumuyeretsa ndipo adzatumikira monga wansembe wanga.

  • Levitiko 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mkulu wa ansembe wokhala pakati pa abale ake ansembe, amene anamuthira mafuta odzozera unsembe pamutu pake,+ nʼkuikidwa kukhala wansembe* kuti azivala zovala zaunsembe,+ asalekerere tsitsi lake osalisamala ndipo asangʼambe zovala zake.+

  • Salimo 133:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Zili ngati mafuta abwino amene athiridwa pamutu+

      Amene akuyenderera pandevu,

      Ndevu za Aroni,+

      Ndipo akuyenderera mpaka mʼkolala ya zovala zake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena