Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nyimbo ya Solomo 3
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Zimene Zili Mʼbuku la Nyimbo ya Solomo

    • MSULAMI ALI MUMSASA WA MFUMU SOLOMO (1:1–3:5)

    • MSULAMI ALI KU YERUSALEMU (3:6–8:4)

        • Ana aakazi a Ziyoni (6-11)

          • Gulu la anthu limene linkayenda ndi Solomo

Nyimbo ya Solomo 3:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 1:7
  • +Nym 5:6

Nyimbo ya Solomo 3:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 5:7

Nyimbo ya Solomo 3:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 8:2

Nyimbo ya Solomo 3:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 2:7; 8:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, tsa. 31

    11/15/2006, ptsa. 18-19

    11/15/1987, ptsa. 24-25

Nyimbo ya Solomo 3:6

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 30:23, 24, 34

Nyimbo ya Solomo 3:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 9:22

Nyimbo ya Solomo 3:9

Mawu a M'munsi

  • *

    Limeneli linali bedi lochita kunyamula limene ankanyamulirapo munthu wolemekezeka.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 5:8, 9

Nyimbo ya Solomo 3:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 12:24; Miy 4:3

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Nyimbo 3:1Nym 1:7
Nyimbo 3:1Nym 5:6
Nyimbo 3:3Nym 5:7
Nyimbo 3:4Nym 8:2
Nyimbo 3:5Nym 2:7; 8:4
Nyimbo 3:6Eks 30:23, 24, 34
Nyimbo 3:71Mf 9:22
Nyimbo 3:91Mf 5:8, 9
Nyimbo 3:112Sa 12:24; Miy 4:3
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Nyimbo ya Solomo 3:1-11

Nyimbo ya Solomo

3 “Ndili pabedi panga usiku,

Ndinaganizira za munthu amene ndimamukonda.+

Ndinamufunafuna koma sindinamupeze.+

 2 Choncho ndinati: ‘Ndidzuka nʼkukazungulira mumzinda,

Mʼmisewu ndi mʼmabwalo amumzinda,

Kuti ndikafunefune munthu amene ndimamukonda.’

Ndinamufunafuna koma sindinamupeze.

 3 Alonda amene ankazungulira mumzindawo anandipeza.+

Ndipo ine ndinawafunsa kuti: ‘Kodi mwamuonako munthu amene ndimamukonda?’

 4 Nditangowapitirira pangʼono,

ndinamʼpeza munthu amene ndimamukonda.

Ndinamugwira ndipo sindinafune kumʼsiya

Mpaka nditamubweretsa mʼnyumba ya mayi anga,+

Mʼchipinda chamkati cha mayi amene anali ndi pakati kuti ine ndibadwe.

 5 Ndakulumbiritsani inu ana aakazi a ku Yerusalemu,

Pali insa ndiponso pali mphoyo zakutchire kuti:

Musayese kudzutsa chikondi mwa ine nthawi yake isanakwane.”+

 6 “Kodi chinthu chikuchokera kuchipululuchi nʼchiyani, chooneka ngati utsi wokwera mʼmwamba,

Chonunkhira mafuta a mule ndi lubani,*

Komanso ndi zonunkhira zonse za ufa za munthu wamalonda?”+

 7 “Taonani! Ndi bedi la Solomo.

Lazunguliridwa ndi amuna 60 amphamvu,

Ochokera mwa amuna amphamvu a mu Isiraeli,+

 8 Onsewo atenga malupanga,

Ndipo onse ndi ophunzitsidwa nkhondo,

Aliyense wamangirira lupanga lake mʼchiuno

Kuti adziteteze ku zinthu zoopsa za usiku.”

 9 “Ndi bedi* lachifumu la Mfumu Solomo

Limene anapanga yekha ndi mitengo ya ku Lebanoni.+

10 Zipilala zake ndi zasiliva,

Motsamira mwake ndi mwagolide.

Chokhalira chake ndi chopangidwa ndi ubweya wa nkhosa wapepo.

Mkati mwake, ana aakazi a ku Yerusalemu

Anakongoletsamo posonyeza chikondi.”

11 “Tulukani, inu ana aakazi a Ziyoni,

Pitani mukaone Mfumu Solomo

Itavala nkhata yamaluwa, imene mayi ake+ anailukira

Kuti ivale pa tsiku la ukwati wake,

Pa tsiku limene mtima wa mfumuyo unasangalala.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena