Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 34:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma pa tsiku lachitatu, pamene anthuwo anali pa ululu,+ ana awiri a Yakobo, Simiyoni ndi Levi,+ alongo ake a Dina,+ aliyense anatenga lupanga lake n’kukalowa mumzindawo mosaonetsera cholinga chawo. Kenako anayamba kupha mwamuna aliyense.+

  • Genesis 42:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndiyeno Yosefe anapita payekha kukalira.+ Kenako anabwerako n’kuyambiranso kulankhula nawo, ndipo anatenga Simiyoni+ n’kumumanga iwo akuona.+

  • Genesis 49:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Simiyoni ndi Levi m’pachibale pawo.+ Malupanga awo ndiwo zida zochitira zachiwawa.+

  • 1 Mbiri 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ana a Simiyoni anali Nemueli,+ Yamini,+ Yaribi, Zera, ndi Shauli.+

  • Chivumbulutso 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mu fuko la Simiyoni,+ 12,000.

      Mu fuko la Levi,+ 12,000.

      Mu fuko la Isakara,+ 12,000.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena