Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawiyi n’kuti Labani atapita kukameta ubweya wa nkhosa zake. Akali kumeneko, Rakele anaba aterafi*+ a bambo ake.

  • Genesis 35:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Yakobo anauza anthu a m’banja lake ndi onse amene anali naye kuti: “Chotsani milungu yachilendo imene ili pakati panu.+ Dziyeretseni ndipo sinthani zovala zanu.+

  • Oweruza 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Poyankha, iye anati: “Mwatenga milungu yanga+ imene ndinapanga,+ ndipo mwatenganso wansembe+ n’kumapita naye. Nanga ine nditsala ndi chiyani?+ Ndiye mungandifunse bwanji kuti, ‘Vuto lako n’chiyani?’”

  • Yesaya 37:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kodi milungu+ ya mitundu imene makolo anga anaiwononga inawalanditsa?+ Kodi inalanditsa Gozani,+ Harana,+ Rezefi ndi ana a Edeni+ amene anali ku Tela-sara?

  • Machitidwe 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Tsopano mukuona ndipo mukumva za Paulo ameneyu, kuti si mu Efeso+ mokha muno mmene wakopa anthu ambirimbiri ndi kuwapatutsira ku chikhulupiriro china. Wachita zimenezi pafupifupi m’chigawo chonse cha Asia. Iye akumanena kuti milungu yopangidwa ndi manja+ si milungu ayi.

  • 1 Akorinto 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiye chifukwa chake, okondedwa anga, thawani+ kupembedza mafano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena