Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Usaziweramire kapena kuzitumikira,+ chifukwa ine Yehova Mulungu wako, ndine Mulungu wofuna kuti anthu azidzipereka kwa ine ndekha,*+ wolanga ana, zidzukulu ndi ana a zidzukuluzo,* chifukwa cha zolakwa za anthu odana ndi ine.+

  • Maliro 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Maso anga atopa ndi kulira.+ M’mimba mwanga mukubwadamuka.+

      Chiwindi changa chakhuthulidwa+ pansi chifukwa cha kuwonongedwa kwa mwana wamkazi wa anthu anga,+

      Ndiponso chifukwa chakuti ana ndi makanda oyamwa akukomoka+ m’mabwalo a mzinda.

  • Maliro 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nyamuka! Lira mofuula usiku, pa nthawi yoyamba ulonda+ wam’mawa.

      Khuthula+ mtima wako pamaso+ pa Yehova ngati madzi.

      Pemphera utakweza manja+ ako kwa iye chifukwa cha ana ako,

      Amene akukomoka ndi njala m’misewu.+

  • Maliro 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ngakhale amayi, amene amakhala achifundo, afika pophika ana awo ndi manja awo.+

      Anawo akhala ngati chakudya chotonthoza anthu pa nthawi ya kuwonongedwa kwa mwana wamkazi wa anthu anga.+

  • Hoseya 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti ngakhale alere ana awo, ine ndidzawaphera anawo moti sadzakula n’kukhala amuna.+ Tsoka kwa iwo ndikadzawachokera!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena