Genesis 38:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Patapita miyezi itatu, Yuda anauzidwa kuti: “Tamara mpongozi wako anachita chiwerewere,+ ndipo ali ndi pakati.”+ Yuda atamva zimenezo, anati: “M’tulutseni kuti aphedwe ndi kuotchedwa.”+ Levitiko 20:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “‘Mwamuna akakwatira mkazi n’kugonanso ndi mayi a mkaziyo, limenelo ndi khalidwe lotayirira.+ Aziphedwa ndi kutenthedwa,+ onse mwamunayo ndi akaziwo, kuti khalidwe lotayirira+ lisapitirire pakati panu. Levitiko 21:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “‘Mwana wamkazi wa wansembe akadziipitsa mwa kuchita uhule, pamenepo waipitsa bambo ake. Aziphedwa ndi kutenthedwa.+ Yoswa 7:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Amene apezeke ndi zinthu zoyenera kuwonongedwazo, adzatenthedwa ndi moto,+ iye limodzi ndi banja lake ndi zonse ali nazo. Adzatenthedwa chifukwa waphwanya pangano la Yehova,+ ndiponso wachita cholakwa chochititsa manyazi mu Isiraeli.”’”+
24 Patapita miyezi itatu, Yuda anauzidwa kuti: “Tamara mpongozi wako anachita chiwerewere,+ ndipo ali ndi pakati.”+ Yuda atamva zimenezo, anati: “M’tulutseni kuti aphedwe ndi kuotchedwa.”+
14 “‘Mwamuna akakwatira mkazi n’kugonanso ndi mayi a mkaziyo, limenelo ndi khalidwe lotayirira.+ Aziphedwa ndi kutenthedwa,+ onse mwamunayo ndi akaziwo, kuti khalidwe lotayirira+ lisapitirire pakati panu.
9 “‘Mwana wamkazi wa wansembe akadziipitsa mwa kuchita uhule, pamenepo waipitsa bambo ake. Aziphedwa ndi kutenthedwa.+
15 Amene apezeke ndi zinthu zoyenera kuwonongedwazo, adzatenthedwa ndi moto,+ iye limodzi ndi banja lake ndi zonse ali nazo. Adzatenthedwa chifukwa waphwanya pangano la Yehova,+ ndiponso wachita cholakwa chochititsa manyazi mu Isiraeli.”’”+