Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 11:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 M’dziko la ana a Isiraeli, palibe Aanaki amene anatsalamo,+ kupatulapo okhala ku Gaza,+ ku Gati+ ndi ku Asidodi.+

  • 1 Samueli 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndiyeno zifanizo zagolide za matenda a mudzi zimene Afilisiti anapereka kwa Yehova monga nsembe ya kupalamula ndi izi:+ mzinda wa Asidodi+ unapereka chifanizo chimodzi, wa Gaza+ chimodzi, wa Asikeloni+ chimodzi, wa Gati+ chimodzi ndi wa Ekironi+ chimodzi.

  • Machitidwe 8:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Koma Filipo anapezeka ali ku Asidodi, ndipo anayendayenda m’deralo ndi kulengeza+ uthenga wabwino m’mizinda yonse mpaka anafika ku Kaisareya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena