Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsopano Afilisiti anatenga likasa+ la Mulungu woona kuchoka nalo ku Ebenezeri n’kupita nalo ku Asidodi.+

  • 2 Mbiri 26:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye anapita kukamenyana ndi Afilisiti+ ndipo anagumula mpanda wa ku Gati,+ wa ku Yabine+ ndi wa ku Asidodi.+ Kenako anamanga mizinda m’chigawo cha Asidodi+ ndiponso pakati pa Afilisiti.

  • Yeremiya 25:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 khamu lonse la anthu a mitundu yosiyanasiyana, mafumu onse a dziko la Uzi,+ mafumu onse a dziko la Afilisiti,+ Asikeloni,+ Gaza,+ Ekironi+ ndi otsala onse a ku Asidodi,+

  • Zekariya 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mwana wochokera mu mtundu wina wa anthu+ adzakhala mu Asidodi,+ ndipo ine ndidzathetsa kunyada kwa Afilisiti.+

  • Machitidwe 8:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Koma Filipo anapezeka ali ku Asidodi, ndipo anayendayenda m’deralo ndi kulengeza+ uthenga wabwino m’mizinda yonse mpaka anafika ku Kaisareya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena