Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 71:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ngakhale nditakalamba ndi kumera imvi, inu Mulungu musandisiye,+

      Kufikira nditanena za dzanja lanu lamphamvu ku m’badwo wotsatira,+

      Kufikira nditanena za mphamvu zanu kwa onse obwera m’tsogolo.+

  • Miyambo 16:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Imvi ndizo chisoti chachifumu cha ulemerero+ zikapezeka m’njira yachilungamo.+

  • Miyambo 20:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kukongola kwa anyamata ndiko mphamvu zawo,+ ndipo ulemerero wa anthu okalamba ndiwo imvi zawo.+

  • Yesaya 46:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ine sindisintha ngakhale kwa wokalamba,+ ndipo munthu wa imvi ndimamunyamula nthawi zonse.+ Ndithu ineyo ndidzachitapo kanthu+ kuti ndiwatenge, ndiwanyamule ndi kuwapulumutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena