Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Umenewu ndiwo mzere wa Aroni ndi Mose, amene Yehova anawauza kuti:+ “Tulutsani ana a Isiraeli m’dziko la Iguputo malinga ndi makamu awo.”+

  • Nehemiya 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Munawaphunzitsa za sabata lanu lopatulika.+ Munawapatsa malangizo, mfundo ndi chilamulo kudzera mwa Mose mtumiki wanu.+

  • Salimo 77:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwatsogolera anthu anu ngati nkhosa,+

      Kudzera mwa Mose ndi Aroni.+

  • Salimo 105:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno anatumiza Mose mtumiki wake,+

      Ndi Aroni amene anamusankha.+

  • Hoseya 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova anatulutsa Isiraeli ku Iguputo pogwiritsa ntchito mneneri,+ ndipo mneneri analondera Isiraeli.+

  • Mika 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ine ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo,+ ndipo ndinakuwombolani m’nyumba ya akapolo.+ Ndinakutumizirani Mose, Aroni ndi Miriamu kuti akutsogolereni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena