Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Davide anayamba kufunsa amuna amene anali ataimirira pafupi naye kuti: “Kodi munthu amene angakaphe Mfilisiti+ ameneyu ndi kuchotsa chitonzo pa Isiraeli+ amuchitira chiyani? Kodi Mfilisiti wosadulidwa+ ameneyu ndani kuti azinyoza+ asilikali a Mulungu wamoyo?”+

  • 2 Mafumu 19:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kodi ndani amene iwe wamutonza+ ndi kumulankhula monyoza?+

      Ndipo ndani amene iwe wam’kwezera mawu,+

      Ndi kum’kwezera maso ako m’mwamba?+

      Ndi Woyera wa Isiraeli!+

  • Salimo 80:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mwachititsa kuti anthu oyandikana nafe azimenyana polimbirana ifeyo.+

      Ndipo adani athu akupitirizabe kutinyoza mmene akufunira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena