Genesis 19:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Nayenso mwana wamng’onoyo anabereka mwana wamwamuna, n’kumutcha dzina lakuti Beni-ami. Iye ndiye tate wa ana a Amoni+ mpaka lero. Oweruza 10:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pamenepo, mkwiyo wa Yehova unayakira ana a Isiraeli,+ moti anawagulitsa+ kwa Afilisiti+ ndi kwa ana a Amoni.+ Oweruza 11:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Kenako Yefita anatumiza mithenga kwa mfumu ya ana a Amoni+ kuti: “Ndili nanu chiyani inu,+ kuti mubwere kudzamenyana nane m’dziko langa?” Oweruza 11:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Iye anakantha ana a Amoni kuyambira ku Aroweli mpaka kukafika ku Miniti,+ mizinda 20. Anawakantha koopsa mpaka kukafika ku Abele-kerami. Choncho ana a Amoni anagonja pamaso pa ana a Isiraeli. 1 Samueli 11:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndiyeno Nahasi Muamoni+ anapita kukamanga msasa kuti amenyane ndi mzinda wa Yabesi+ ku Giliyadi. Zitatero, amuna onse a ku Yabesi anauza Nahasi kuti: “Chita nafe pangano kuti tizikutumikira.”+
38 Nayenso mwana wamng’onoyo anabereka mwana wamwamuna, n’kumutcha dzina lakuti Beni-ami. Iye ndiye tate wa ana a Amoni+ mpaka lero.
7 Pamenepo, mkwiyo wa Yehova unayakira ana a Isiraeli,+ moti anawagulitsa+ kwa Afilisiti+ ndi kwa ana a Amoni.+
12 Kenako Yefita anatumiza mithenga kwa mfumu ya ana a Amoni+ kuti: “Ndili nanu chiyani inu,+ kuti mubwere kudzamenyana nane m’dziko langa?”
33 Iye anakantha ana a Amoni kuyambira ku Aroweli mpaka kukafika ku Miniti,+ mizinda 20. Anawakantha koopsa mpaka kukafika ku Abele-kerami. Choncho ana a Amoni anagonja pamaso pa ana a Isiraeli.
11 Ndiyeno Nahasi Muamoni+ anapita kukamanga msasa kuti amenyane ndi mzinda wa Yabesi+ ku Giliyadi. Zitatero, amuna onse a ku Yabesi anauza Nahasi kuti: “Chita nafe pangano kuti tizikutumikira.”+