Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Utalikirane ndi mawu onama.+ Usaphe munthu wosalakwa ndi munthu wolungama, chifukwa woipa sindidzamuyesa wolungama.+

  • 2 Samueli 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiye kuli bwanji pamene anthu oipa+ apha munthu wolungama pabedi m’nyumba yake? Kodi sindiyenera kufuna magazi ake m’manja mwanu+ ndi kukuchotsani padziko?”+

  • 2 Mbiri 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 koma wayenda m’njira ya mafumu a Isiraeli+ n’kuchititsa Yuda ndi anthu okhala mu Yerusalemu kuchita zoipa,+ monga mmene a m’nyumba ya Ahabu anachititsira ena kuchita zoipa,+ ndiponso wapha ngakhale abale ako a m’nyumba ya bambo ako amene anali abwino kuposa iwe,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena