-
1 Mafumu 6:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 Zitseko ziwirizo zinali za matabwa a mtengo wa mafuta. Pazitsekopo anajambulapo mochita kugoba akerubi, mitengo ya kanjedza, ndi maluwa, ndipo anazikuta ndi golide. Kenako akerubi ndi mitengo ya kanjedza yolemba mochita kugoba ya pazitsekozo, anazikuta ndi golide.
-