Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 4:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Nthawi yomweyo Elisa anauza Gehazi+ kuti: “Kokera chovala chako m’chiuno ndipo uchimange.+ Tenga ndodo yangayi+ uzipita. Ukakumana ndi munthu aliyense panjira usamupatse moni,+ ndipo munthu akakupatsa moni, usamuyankhe. Ukaike ndodo yangayi pankhope ya mwanayo.”+

  • 2 Mafumu 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Gehazi,+ amene anali kutumikira Elisa, munthu wa Mulungu woona+ uja, ananena mumtima mwake kuti: “Mbuyanga wangomusiya Namani+ Msiriya uja osalandira zimene anabweretsa. Pali Yehova Mulungu wamoyo,+ ndim’thamangira kuti ndikatengeko zinthu zina kwa iye.”+

  • 2 Mafumu 5:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Tsopano khate+ la Namani limamatira iweyo ndi mbadwa zako mpaka kalekale.”*+ Nthawi yomweyo Gehazi anachoka pamaso pa Elisa, atachita khate loyera kuti mbuu.+

  • 2 Mafumu 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa nthawiyo, mfumu inali ikulankhula ndi Gehazi+ mtumiki wa munthu wa Mulungu woona, kuti: “Ndifotokozere zinthu zonse zazikulu zimene Elisa wachita.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena