-
2 Mafumu 2:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Elisa atamva zimenezi ananena kuti: “Ndibweretsereni mbale yaing’ono yatsopano yolowa, ndipo muikemo mchere.” Anthuwo anam’bweretseradi mbaleyo.
-
-
2 Mafumu 4:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Ukakatero, iwe ndi ana akowo mukalowe m’nyumba ndipo mukatseke chitseko. Ndiyeno uzikathira mafutawo m’zotengerazo. Zimene zadzaza uzikaziika pambali.”
-
-
2 Mafumu 7:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Tsopano Elisa anati: “Amuna inu, mverani mawu a Yehova.+ Yehova wanena kuti, ‘Mawa chapanthawi ngati ino, pachipata cha Samariya, ufa wosalala wokwana muyezo umodzi wa seya,* mtengo wake udzakhala sekeli* limodzi, ndipo balere wokwana miyezo iwiri ya seya, mtengo wake udzakhalanso sekeli limodzi.’”+
-