-
2 Mafumu 3:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Atamva zimenezo, Yehosafati anati: “Mawu a Yehova ali mwa iye.” Choncho mfumu ya Isiraeli, Yehosafati, ndi mfumu ya Edomu, anapita kwa Elisa.
-
-
2 Mafumu 6:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 Tsopano Elisa anali atakhala m’nyumba mwake pamodzi ndi akulu+ pamene mfumu inatumiza mthenga kwa iye. Mthengayo asanafike, Elisa anauza akuluwo kuti: “Kodi mwaona kuti mwana wa munthu wopha anthu+ uja watumiza munthu kuti adzandidule mutu? Muonetsetse kuti mthengayo akangofika mutseke chitseko ndipo muchitsamire kuti asathe kulowa. Kodi mapazi a mbuye wake si amene akumveka+ pambuyo pakewo?”
-