-
2 Mafumu 22:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 “Pitani mukafunse+ kwa Yehova m’malo mwa ineyo, m’malo mwa anthuwa, ndi m’malo mwa Yuda yense. Mukafunse zokhudza mawu a m’buku limene lapezekali, chifukwa mkwiyo wa Yehova+ umene watiyakira ndi waukulu, popeza makolo+ athu sanamvere mawu a m’buku ili. Iwo sanachite zonse zimene zalembedwamo zokhudza ife.”+
-