Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno ana amene anali m’mimba mwake anayamba kulimbana,+ moti iye anati: “Ngati umu ndi mmene ndivutikire, ndiye ndi bwino ndingofa.” Atatero anapita kukafunsira kwa Yehova.+

  • 1 Mafumu 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Yerobowamu anauza mkazi wake kuti: “Nyamuka, udzisinthe+ kuti anthu asadziwe kuti ndiwe mkazi wa Yerobowamu ndipo upite ku Silo. Kumeneko n’kumene kuli mneneri Ahiya.+ Ameneyo ndiye anandiuza kuti ndidzakhala mfumu ya anthuwa.+

  • 2 Mafumu 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo Yehosafati anati:+ “Kodi kuno kulibe mneneri wa Yehova?+ Ngati alipo tiyeni tifunsire kwa Yehova kudzera mwa iye.”+ Ndiyeno mmodzi mwa atumiki a mfumu ya Isiraeli anayankha kuti: “Kuli Elisa+ mwana wa Safati, amene anali kuthirira Eliya madzi osamba m’manja.”+

  • 2 Mafumu 22:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Pitani mukafunse+ kwa Yehova m’malo mwa ineyo, m’malo mwa anthuwa, ndi m’malo mwa Yuda yense. Mukafunse zokhudza mawu a m’buku limene lapezekali, chifukwa mkwiyo wa Yehova+ umene watiyakira ndi waukulu, popeza makolo+ athu sanamvere mawu a m’buku ili. Iwo sanachite zonse zimene zalembedwamo zokhudza ife.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena