1 Mafumu 19:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Kenako Yehova anamuuza kuti: “Nyamuka, bwerera udzere kuchipululu cha Damasiko.+ Pita ukadzoze+ Hazaeli+ kuti akhale mfumu ya Siriya. 2 Mafumu 8:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Hazaeli atamva mawu amenewa, anati: “Ndine ndani ine mtumiki wanu, galu ngati ine,+ kuti ndichite zinthu zazikulu ngati zimenezi?” Koma Elisa anati: “Yehova wandionetsa iweyo utakhala mfumu ya Siriya.”+ 2 Mafumu 10:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 M’masiku amenewo, Yehova anayamba kulanda dziko la Isiraeli pang’ono ndi pang’ono, ndipo Hazaeli+ anapitiriza kupha anthu m’madera onse a dziko la Isiraeli. Amosi 1:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndidzatumiza moto+ panyumba ya Hazaeli,+ ndipo udzanyeketsa nsanja zokhalamo za Beni-hadadi.+
15 Kenako Yehova anamuuza kuti: “Nyamuka, bwerera udzere kuchipululu cha Damasiko.+ Pita ukadzoze+ Hazaeli+ kuti akhale mfumu ya Siriya.
13 Hazaeli atamva mawu amenewa, anati: “Ndine ndani ine mtumiki wanu, galu ngati ine,+ kuti ndichite zinthu zazikulu ngati zimenezi?” Koma Elisa anati: “Yehova wandionetsa iweyo utakhala mfumu ya Siriya.”+
32 M’masiku amenewo, Yehova anayamba kulanda dziko la Isiraeli pang’ono ndi pang’ono, ndipo Hazaeli+ anapitiriza kupha anthu m’madera onse a dziko la Isiraeli.