1 Samueli 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndiyeno Hana anayamba kupemphera+ kuti:“Mtima wanga ukukondwera mwa Yehova,+Nyanga* yanga yakwezekadi kudzera mwa Yehova.+Ndikutsutsana ndi adani anga molimba mtima,Pakuti ndikukondwera ndi chipulumutso chochokera kwa inu.+ Nehemiya 12:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Pa tsiku limenelo anapereka nsembe zochuluka+ ndipo anasangalala+ pakuti Mulungu woona anawachititsa kusangalala kwambiri.+ Akazi+ ndi ana+ nawonso anasangalala, mwakuti phokoso la chisangalalo cha Yerusalemu linamveka kutali.+ Salimo 20:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+ Salimo 30:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Ndidzakutamandani inu Yehova, pakuti mwandipulumutsa,+Ndipo simunalole kuti adani anga akondwere ndi kusautsika kwanga.+
2 Ndiyeno Hana anayamba kupemphera+ kuti:“Mtima wanga ukukondwera mwa Yehova,+Nyanga* yanga yakwezekadi kudzera mwa Yehova.+Ndikutsutsana ndi adani anga molimba mtima,Pakuti ndikukondwera ndi chipulumutso chochokera kwa inu.+
43 Pa tsiku limenelo anapereka nsembe zochuluka+ ndipo anasangalala+ pakuti Mulungu woona anawachititsa kusangalala kwambiri.+ Akazi+ ndi ana+ nawonso anasangalala, mwakuti phokoso la chisangalalo cha Yerusalemu linamveka kutali.+
5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+
30 Ndidzakutamandani inu Yehova, pakuti mwandipulumutsa,+Ndipo simunalole kuti adani anga akondwere ndi kusautsika kwanga.+