Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo Yonatani anati: “N’zosatheka kuti iwe ukhale wolakwa! Koma ngati ndingadziwe zoipa zimene bambo anga akufuna kukuchitira, ukuganiza kuti sindingakuuze?”+

  • 1 Samueli 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho mudziwe zimenezi ndi kuona zimene mungachite, chifukwa atsimikiza kudzetsa tsoka+ pa mbuyanga ndi onse a m’nyumba yake, pakuti mbuye wathu ndi munthu wopanda pake,+ sitingathe kulankhula naye.”

  • Salimo 112:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Woipa adzaona zimenezi ndipo adzasautsika.+

      ש [Shin]

      Adzakukuta mano ndi kusungunuka.+

      ת [Taw]

      Chikhumbo cha anthu oipa chidzatha.+

  • Miyambo 19:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango wamphamvu,+ koma kukoma mtima kwake kuli ngati mame pazomera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena