Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Adzachititsa ofatsa kutsatira zigamulo zake,+

      Ndipo adzaphunzitsa ofatsa kuyenda m’njira yake.+

  • Salimo 32:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu munati: “Ndidzakupatsa nzeru ndi kukulangiza njira yoti uyendemo.+

      Ndidzakupatsa malangizo ndi kukuyang’anira.+

  • Salimo 37:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova walimbitsa mapazi a munthu wamphamvu zake,+

      Ndipo Mulungu amakondwera ndi njira zake.+

  • Salimo 143:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiphunzitseni kuchita chifuniro chanu,+

      Pakuti inu ndinu Mulungu wanga.+

      Mzimu wanu ndi wabwino.+

      Unditsogolere m’dziko la olungama.+

  • Miyambo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Uzim’kumbukira m’njira zako zonse,+ ndipo iye adzawongola njira zako.+

  • Yesaya 58:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Mukatero kuwala kwanu kudzaonekera ngati m’bandakucha,+ ndipo mudzachira mofulumira kwambiri.+ Chilungamo chanu chizidzayenda patsogolo panu,+ ndipo ulemerero wa Yehova uzidzalondera kumbuyo kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena