Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mafumu a dziko lapansi aima pamalo awo,+

      Ndipo nduna zapamwamba zasonkhana pamodzi mogwirizana.+

      Atero kuti alimbane ndi Yehova+ komanso wodzozedwa wake.+

  • Salimo 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 M’kamwa mwa ana aang’ono ndi ana oyamwa mwakhazikitsamo zamphamvu,+

      Chifukwa cha amene akukuchitirani zoipa.+

      Mwatero kuti mugonjetse mdani wanu komanso amene akufuna kukubwezerani zoipa.+

  • Salimo 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Zochita zake zimayenda bwino nthawi zonse.+

      Zigamulo zanu zili pamwamba kwambiri pamene iye sangathe kuziona.+

      Onse omuchitira zoipa amawanyodola.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena