Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Asa anamukwiyira wamasomphenyayo. Kenako anamuika m’ndende n’kumumanga m’matangadza+ popeza anamupsera mtima kwambiri chifukwa cha nkhani imeneyi.+ Pa nthawi yomweyo, Asa anayamba kuponderezanso+ anthu ake ena.

  • 2 Mbiri 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Poyankha, mfumu ya Isiraeli inauza Yehosafati+ kuti: “Pali munthu mmodzi+ amene tingathe kufunsira kwa Yehova kudzera mwa iye, koma ineyo ndimadana naye+ kwambiri, chifukwa masiku ake onse salosera zabwino zokhudza ine, koma zoipa zokhazokha.+ Munthuyo dzina lake ndi Mikaya mwana wa Imula.”+ Koma Yehosafati anati: “Musalankhule choncho mfumu.”+

  • 2 Mbiri 24:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova anapitiriza kutumiza aneneri+ pakati pawo kuti awabwezere kwa iye. Aneneriwo anapitiriza kupereka umboni wowatsutsa, koma sanamvere.+

  • Yeremiya 11:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho Yehova wanena motsutsana ndi anthu a ku Anatoti+ amene akufuna moyo wako, ndipo akunena kuti: “Usanenere m’dzina la Yehova,+ ngati ukufuna kuti tisakuphe.”

  • Yeremiya 26:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo ansembe ndi aneneri anayamba kuuza akalongawo ndi anthu onse kuti: “Munthu uyu akuyenera chiweruzo cha imfa+ chifukwa chakuti wanenera za mzinda uwu monga mmene mwamvera ndi makutu anu.”+

  • Machitidwe 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Komabe, kuti nkhaniyi isapitirire kufalikira kwa anthu ena, tiyeni tiwaopseze kuti asalankhulenso m’dzina limeneli kwa munthu wina aliyense.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena