-
Oweruza 17:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Ndiyeno anabweza ndalama zasiliva zokwana 1,100 zija kwa mayi ake.+ Atabweza ndalamazo, mayi akewo anati: “Ndithudi ndipereka ndalama zasilivazi kwa Yehova kuti zikhale zopatulika. Ndichita zimenezi kuti ndithandize mwana wanga, ndi kuti papangidwe chifaniziro chosema+ ndiponso chifaniziro chopangidwa ndi chitsulo chosungunula.+ Tsopano ndikubweza ndalamazi kwa iwe.”
-