Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Koma iwe Yuda,+ abale ako adzakutamanda.+ Dzanja lako lidzakhala pambuyo pa khosi la adani ako.+ Ana a bambo ako adzakugwadira.+

  • 1 Mbiri 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chifukwa chakuti Yuda+ anali wamphamvu pakati pa abale ake, mwa iye munachokera mtsogoleri,+ koma udindo wa woyamba kubadwa unali wa Yosefe.+

  • 1 Mbiri 28:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komabe, m’nyumba yonse ya bambo anga+ Yehova Mulungu wa Isiraeli anasankha ineyo kuti ndikhale mfumu+ ya Isiraeli mpaka kalekale, popeza anasankha Yuda kuti akhale mtsogoleri.+ M’nyumba ya Yuda anasankhamo nyumba ya bambo anga.+ Pa ana a bambo anga+ anavomereza ineyo+ kuti ndikhale mfumu ya Isiraeli yense.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena