32 “Ine ndikutsutsana ndi aneneri amene akulota maloto onama, amene akunena malotowo ndi kusocheretsa anthu anga ndi bodza lawo+ komanso ndi kudzitama kwawo,”+ watero Yehova.
“Koma ine sindinawatume kapena kuwalamula kuchita zimenezo. Choncho sadzachita zopindulitsa anthu awa,”+ watero Yehova.