Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pa nkhondoyo iwo anathandizidwa moti Ahagara ndi onse amene anali nawo anaperekedwa m’manja mwawo, popeza anapempha Mulungu kuti awathandize+ ndipo iye anamva kupembedzera kwawo chifukwa anam’khulupirira.+

  • Salimo 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.+

      Madalitso anu ali pa anthu anu.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 22:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Makolo athu anali kudalira inu.+

      Iwo anali kudalira inu ndipo munali kuwapulumutsa.+

  • Salimo 91:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mulungu wanena kuti: “Popeza wasonyeza kuti amandikonda,+

      Inenso ndidzamupulumutsa.+

      Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa.+

  • 2 Akorinto 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ngakhalenso m’mitima mwathu, tinali kumva ngati talandira chiweruzo cha imfa. Zinatero kuti tisakhale ndi chikhulupiriro mwa ife tokha,+ koma mwa Mulungu amene amaukitsa akufa.+

  • Aheberi 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiponso, popanda chikhulupiriro+ n’zosatheka kukondweretsa Mulungu.+ Pakuti aliyense wofika kwa Mulungu ayenera kukhulupirira kuti iye alikodi,+ ndi kuti amapereka mphoto+ kwa anthu omufunafuna ndi mtima wonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena