Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anthu a mitundu ina adzawatenga n’kubwerera nawo kwawo ndipo nyumba ya Isiraeli idzatenga anthuwo kuti akhale awo m’dziko la Yehova, ndiponso kuti akhale antchito awo aamuna ndi aakazi.+ Iwo adzagwira+ anthu amene anawagwira n’kupita nawo kudziko lina ndipo azidzalamulira anthu amene anali kuwagwiritsa ntchito.+

  • Danieli 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno mfumuyo inafuula kuti aibweretsere olankhula ndi mizimu, Akasidi* ndi okhulupirira nyenyezi.+ Mfumuyo inauza amuna anzeru a m’Babulo amenewa kuti: “Aliyense amene angawerenge mawuwa ndi kundiuza kumasulira kwake, ndimuveka zovala zofiirira*+ ndi mkanda wagolide m’khosi, ndipo ndimuika kukhala wolamulira wachitatu mu ufumuwu.”+

  • Danieli 5:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndamvanso kuti iweyo umatha kumasulira zinthu+ ndi kumasula mfundo. Tsopano ngati ungathe kuwerenga mawuwa ndi kundiuza kumasulira kwake, ndikuveka zovala zofiirira ndi mkanda wagolide m’khosi, ndipo ndikuika kukhala wolamulira wachitatu mu ufumuwu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena