Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pamenepo Balamu anayamba kulankhula mwa ndakatulo,+ kuti:

      “Balaki mfumu ya Mowabu yandiitana kuchokera ku Aramu,+

      Kuchokera kumapiri a kum’mawa, kuti:

      ‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.

      Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+

  • Numeri 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Balaki anapsera mtima Balamu n’kuwomba m’manja.+ Kenako anauza Balamu kuti: “Ndinakuitana kuti udzatemberere+ adani anga, koma iwe wawadalitsa kwambiri katatu konseka!

  • Yoswa 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ine sindinafune kumvera Balamu.+ Chotero, iye anakudalitsani mobwerezabwereza,+ ndipo ine ndinakulanditsani m’manja mwake.+

  • 2 Petulo 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Popeza anasiya njira yowongoka, asocheretsedwa. Atsatira njira ya Balamu+ mwana wa Beori, amene anakonda mphoto ya kuchita zoipa,+

  • Chivumbulutso 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “‘Koma ngakhale zili choncho, ndakupeza ndi milandu ingapo. Iwe kumeneko uli ndi anthu olimbikira chiphunzitso cha Balamu,+ amene anaphunzitsa Balaki+ kuikira ana a Isiraeli chopunthwitsa kuti adye zoperekedwa nsembe kwa mafano ndi kuchita dama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena