Numeri 23:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pamenepo Balamu anayamba kulankhula mwa ndakatulo,+ kuti:“Balaki mfumu ya Mowabu yandiitana kuchokera ku Aramu,+Kuchokera kumapiri a kum’mawa, kuti:‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+ Numeri 24:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Pamenepo Balaki anapsera mtima Balamu n’kuwomba m’manja.+ Kenako anauza Balamu kuti: “Ndinakuitana kuti udzatemberere+ adani anga, koma iwe wawadalitsa kwambiri katatu konseka! Yoswa 24:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ine sindinafune kumvera Balamu.+ Chotero, iye anakudalitsani mobwerezabwereza,+ ndipo ine ndinakulanditsani m’manja mwake.+ 2 Petulo 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Popeza anasiya njira yowongoka, asocheretsedwa. Atsatira njira ya Balamu+ mwana wa Beori, amene anakonda mphoto ya kuchita zoipa,+ Chivumbulutso 2:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “‘Koma ngakhale zili choncho, ndakupeza ndi milandu ingapo. Iwe kumeneko uli ndi anthu olimbikira chiphunzitso cha Balamu,+ amene anaphunzitsa Balaki+ kuikira ana a Isiraeli chopunthwitsa kuti adye zoperekedwa nsembe kwa mafano ndi kuchita dama.+
7 Pamenepo Balamu anayamba kulankhula mwa ndakatulo,+ kuti:“Balaki mfumu ya Mowabu yandiitana kuchokera ku Aramu,+Kuchokera kumapiri a kum’mawa, kuti:‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+
10 Pamenepo Balaki anapsera mtima Balamu n’kuwomba m’manja.+ Kenako anauza Balamu kuti: “Ndinakuitana kuti udzatemberere+ adani anga, koma iwe wawadalitsa kwambiri katatu konseka!
10 Ine sindinafune kumvera Balamu.+ Chotero, iye anakudalitsani mobwerezabwereza,+ ndipo ine ndinakulanditsani m’manja mwake.+
15 Popeza anasiya njira yowongoka, asocheretsedwa. Atsatira njira ya Balamu+ mwana wa Beori, amene anakonda mphoto ya kuchita zoipa,+
14 “‘Koma ngakhale zili choncho, ndakupeza ndi milandu ingapo. Iwe kumeneko uli ndi anthu olimbikira chiphunzitso cha Balamu,+ amene anaphunzitsa Balaki+ kuikira ana a Isiraeli chopunthwitsa kuti adye zoperekedwa nsembe kwa mafano ndi kuchita dama.+