Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Misozi yanga yasanduka chakudya changa usana ndi usiku,+

      Pamene anthu akundifunsa tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Maliro 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Njira zopita ku Ziyoni zikulira, chifukwa palibe amene akupita kuchikondwerero.+

      Zipata zake zonse zasiyidwa.+ Ansembe+ ake akuusa moyo.*

      Anamwali ake agwidwa ndi chisoni,+ ndipo iyeyo akumva kuwawa mumtima.

  • Maliro 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye wapasula chisimba*+ chake ngati chisimba cha m’munda+ ndipo wathetsa zikondwerero zake.

      Yehova wachititsa kuti zikondwerero+ ndi sabata ziiwalike mu Ziyoni,

      Ndipo mu mkwiyo wake waukulu wakana mfumu ndi wansembe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena