Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mafumu a dziko lapansi aima pamalo awo,+

      Ndipo nduna zapamwamba zasonkhana pamodzi mogwirizana.+

      Atero kuti alimbane ndi Yehova+ komanso wodzozedwa wake.+

  • Ezekieli 38:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iwe udzabwera m’dzikolo ngati mphepo yamkuntho.+ Iweyo, magulu ako onse a asilikali, pamodzi ndi anthu ambiri a mitundu ina, mudzaphimba dzikolo ngati mitambo.”’+

  • Mika 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Tsopano mitundu yambiri ya anthu idzasonkhana kuti ikuukire. Mitunduyo ikunena kuti, ‘Tiyeni timuwononge ndipo maso athu aone kuwonongeka kwa Ziyoni.’+

  • Zekariya 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndidzasonkhanitsa mitundu yonse ya anthu kuti imenyane ndi Yerusalemu.+ Mzindawu udzalandidwa,+ katundu wa m’nyumba adzatengedwa ndipo akazi adzagwiriridwa.+ Hafu ya anthu a mumzindawu idzatengedwa kupita kudziko lina,+ koma anthu otsala+ sadzachotsedwa mumzindawu.+

  • Chivumbulutso 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kwenikweni amenewa ndi mauthenga ouziridwa+ ndi ziwanda ndipo amachita zizindikiro.+ Mauthengawo akupita kwa mafumu+ a dziko lonse lapansi+ kumene kuli anthu, kuti awasonkhanitsire pamodzi kunkhondo+ ya tsiku lalikulu+ la Mulungu Wamphamvuyonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena