Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 29:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho muzisunga mawu a pangano ili kuti zonse zimene muzichita zizikuyenderani bwino.+

  • Salimo 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma amakondwera ndi chilamulo cha Yehova,+

      Ndipo amawerenga ndi kusinkhasinkha chilamulo chake usana ndi usiku.+

  • Salimo 112:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 112 Tamandani Ya, anthu inu!+

      א [ʼAʹleph]

      Wodala ndi munthu woopa Yehova,+

      ב [Behth]

      Munthu amene amasangalala kwambiri+ ndi malamulo ake.+

  • Salimo 119:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Odala ndi anthu amene amasunga zikumbutso zake,+

      Amene amayesetsa kumufunafuna ndi mtima wonse.+

  • Yesaya 56:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Wodala ndi munthu amene amachita zimenezi,+ ndiponso mwana wa munthu amene amatsatira zimenezi,+ amene amasunga sabata kuti asalidetse,+ ndiponso amaletsa dzanja lake kuti lisachite choipa chilichonse.+

  • Mateyu 7:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Sikuti aliyense wonena kwa ine kuti, ‘Ambuye, Ambuye,’ adzalowa ufumu wakumwamba ayi, koma yekhayo amene akuchita+ chifuniro cha Atate wanga wakumwamba.+

  • Yakobo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma woyang’anitsitsa m’lamulo langwiro+ limene limabweretsa ufulu, amene amalimbikira kutero, adzakhala wosangalala+ polichita chifukwa chakuti sali wongomva n’kuiwala, koma wochita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena