Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Zimene Zili Mʼbuku la Deuteronomo

      • Nyimbo ya Mose (1-47)

        • Yehova ndi Thanthwe (4)

        • Aisiraeli anaiwala Thanthwe lawo (18)

        • “Kubwezera ndi kwanga” (35)

        • “Inu anthu a mitundu ina, sangalalani limodzi ndi anthu ake” (43)

      • Mose akafera mʼphiri la Nebo (48-52)

Deuteronomo 32:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2020, tsa. 10

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    4/2016, ptsa. 3-4

Deuteronomo 32:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 17:26
  • +1Mb 29:11; Sl 145:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2020, ptsa. 10-11

Deuteronomo 32:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 22:31; Sl 18:2; 19:7; Yak 1:17
  • +Sl 33:5
  • +De 7:9; 1Pe 4:19
  • +De 25:16
  • +Ge 18:25

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Yandikirani, tsa. 112

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/2009, tsa. 14

    9/15/2004, tsa. 27

    3/1/1989, ptsa. 19-22

Deuteronomo 32:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:27; Owe 2:19; Sl 14:1
  • +Yes 1:4
  • +Sl 78:8; Lu 9:41

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/1988, tsa. 10

Deuteronomo 32:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 1:2
  • +Yer 4:22
  • +Eks 4:22; De 32:18; Yes 63:16

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2008, tsa. 5

Deuteronomo 32:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:14; Sl 44:1

Deuteronomo 32:8

Mawu a M'munsi

  • *

    Mabaibulo ena amati, “mitundu ya anthu.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 10:5; Sl 115:16
  • +Ge 11:9
  • +De 2:5, 19; Mac 17:26
  • +Ge 15:18; Eks 23:31

Deuteronomo 32:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; De 7:6
  • +Sl 78:71

Deuteronomo 32:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:14, 15
  • +Yer 2:6
  • +Ne 9:19, 20
  • +Zek 2:8

Deuteronomo 32:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2001, tsa. 9

    6/15/2001, tsa. 26

    6/15/1996, tsa. 11

Deuteronomo 32:12

Mawu a M'munsi

  • *

    Apa akunena Yakobo.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:31
  • +Yes 43:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2001, tsa. 9

    6/15/2001, tsa. 26

Deuteronomo 32:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 33:29
  • +De 8:7, 8

Deuteronomo 32:14

Mawu a M'munsi

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “mafuta a nkhosa zamphongo.”

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “mafuta apaimpso a tirigu.”

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “madzi a zipatso za mphesa.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 147:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2015, tsa. 15

    9/15/2004, tsa. 27

    5/1/1989, tsa. 16

Deuteronomo 32:15

Mawu a M'munsi

  • *

    Kutanthauza “Wolungama.” Limeneli ndi dzina laulemu la Isiraeli.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:20; Ne 9:25
  • +Yes 1:4; Ho 13:6

Deuteronomo 32:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 2:12; 1Mf 14:22; 1Ak 10:21, 22
  • +2Mf 23:13; Eze 8:17

Deuteronomo 32:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 17:7; Sl 106:37; 1Ak 10:20

Deuteronomo 32:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 106:21; Yes 17:10; Yer 2:32
  • +De 4:34

Deuteronomo 32:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 2:14; Sl 78:59

Deuteronomo 32:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:17
  • +De 32:5; Yes 65:2; Mt 17:17
  • +Yes 1:2

Deuteronomo 32:21

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti, “anandichititsa nsanje.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 96:5; 1Ak 10:21, 22
  • +1Sa 12:10, 21
  • +Ho 2:23; Aro 9:25; 11:11; 1Pe 2:10
  • +Aro 10:19

Deuteronomo 32:22

Mawu a M'munsi

  • *

    Amenewa ndi manda a anthu onse. Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mlr 4:11
  • +Amo 9:2

Deuteronomo 32:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:53
  • +De 28:21, 22
  • +Le 26:22

Deuteronomo 32:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mlr 1:20
  • +Eze 7:15
  • +2Mb 36:17; Mlr 2:21

Deuteronomo 32:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 12:22; Eze 20:14
  • +Eks 32:12; Nu 14:15, 16
  • +Sl 115:2

Deuteronomo 32:28

Mawu a M'munsi

  • *

    Mabaibulo ena amati, “wosafuna kumva malangizo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 13:15

Deuteronomo 32:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 81:13
  • +Ho 14:9
  • +Yer 2:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 35

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2008, ptsa. 8-11

    7/1/1999, tsa. 32

Deuteronomo 32:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 24:24
  • +Owe 2:14; 1Sa 12:9

Deuteronomo 32:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 2:2
  • +Eks 14:25; 1Sa 4:8; Eza 1:2, 3

Deuteronomo 32:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yuda 7
  • +Yes 5:4; Yer 2:21

Deuteronomo 32:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 2:5

Deuteronomo 32:35

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nah 1:2; Aro 12:19; Ahe 10:30
  • +Sl 73:12, 18

Deuteronomo 32:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ahe 10:30
  • +Owe 2:18; Sl 90:13; 106:45; 135:14

Deuteronomo 32:37

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 10:14

Deuteronomo 32:38

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti, “imene inkadya nsembe zawo zabwino kwambiri.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ho 2:8; 1Ak 10:20, 21

Deuteronomo 32:39

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 41:4; 48:12
  • +De 4:35
  • +1Sa 2:6; Sl 68:20
  • +2Mb 21:16, 18
  • +Nu 12:13; Yer 17:14
  • +Yes 43:13

Deuteronomo 32:40

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ti 1:17; Chv 10:5, 6

Deuteronomo 32:41

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nah 1:3
  • +Yes 1:24; 59:18

Deuteronomo 32:43

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti, “adzayeretsa dziko la anthu ake.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 12:2, 3; 1Mf 8:43; Aro 3:29; 15:10
  • +2Mf 9:7; Chv 6:10
  • +Mik 5:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/1998, ptsa. 12, 17

    4/15/1991, ptsa. 12-13

Deuteronomo 32:44

Mawu a M'munsi

  • *

    Dzina lakale la Yoswa. Hoshiya ndi chidule cha dzina lakuti Hoshaiya limene limatanthauza kuti, “Wopulumutsidwa ndi Ya; Ya Wapulumutsa.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Chv 15:3
  • +Nu 11:28; De 31:22, 23

Deuteronomo 32:46

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:18
  • +De 6:6, 7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/2001, tsa. 19

    8/15/1988, ptsa. 10-12

Deuteronomo 32:47

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:5; De 30:19; Aro 10:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    2/2023, tsa. 3

    Nsanja ya Olonda,

    4/15/2008, ptsa. 5-6

Deuteronomo 32:49

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 27:12
  • +De 34:1
  • +Ge 10:19; 15:18; Yos 1:3

Deuteronomo 32:50

Mawu a M'munsi

  • *

    Awa ndi mawu okuluwika otanthauza imfa.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:28; 33:38

Deuteronomo 32:51

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:12, 13
  • +Le 22:32; Yes 8:13

Deuteronomo 32:52

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 27:13, 14; De 3:27; 34:4, 5

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 32:3Yoh 17:26
Deut. 32:31Mb 29:11; Sl 145:3
Deut. 32:42Sa 22:31; Sl 18:2; 19:7; Yak 1:17
Deut. 32:4Sl 33:5
Deut. 32:4De 7:9; 1Pe 4:19
Deut. 32:4De 25:16
Deut. 32:4Ge 18:25
Deut. 32:5De 31:27; Owe 2:19; Sl 14:1
Deut. 32:5Yes 1:4
Deut. 32:5Sl 78:8; Lu 9:41
Deut. 32:6Yes 1:2
Deut. 32:6Yer 4:22
Deut. 32:6Eks 4:22; De 32:18; Yes 63:16
Deut. 32:7Eks 13:14; Sl 44:1
Deut. 32:8Ge 10:5; Sl 115:16
Deut. 32:8Ge 11:9
Deut. 32:8De 2:5, 19; Mac 17:26
Deut. 32:8Ge 15:18; Eks 23:31
Deut. 32:9Eks 19:5; De 7:6
Deut. 32:9Sl 78:71
Deut. 32:10De 8:14, 15
Deut. 32:10Yer 2:6
Deut. 32:10Ne 9:19, 20
Deut. 32:10Zek 2:8
Deut. 32:11Eks 19:4
Deut. 32:12De 1:31
Deut. 32:12Yes 43:12
Deut. 32:13De 33:29
Deut. 32:13De 8:7, 8
Deut. 32:14Sl 147:14
Deut. 32:15De 31:20; Ne 9:25
Deut. 32:15Yes 1:4; Ho 13:6
Deut. 32:16Owe 2:12; 1Mf 14:22; 1Ak 10:21, 22
Deut. 32:162Mf 23:13; Eze 8:17
Deut. 32:17Le 17:7; Sl 106:37; 1Ak 10:20
Deut. 32:18Sl 106:21; Yes 17:10; Yer 2:32
Deut. 32:18De 4:34
Deut. 32:19Owe 2:14; Sl 78:59
Deut. 32:20De 31:17
Deut. 32:20De 32:5; Yes 65:2; Mt 17:17
Deut. 32:20Yes 1:2
Deut. 32:21Sl 96:5; 1Ak 10:21, 22
Deut. 32:211Sa 12:10, 21
Deut. 32:21Ho 2:23; Aro 9:25; 11:11; 1Pe 2:10
Deut. 32:21Aro 10:19
Deut. 32:22Mlr 4:11
Deut. 32:22Amo 9:2
Deut. 32:24De 28:53
Deut. 32:24De 28:21, 22
Deut. 32:24Le 26:22
Deut. 32:25Mlr 1:20
Deut. 32:25Eze 7:15
Deut. 32:252Mb 36:17; Mlr 2:21
Deut. 32:271Sa 12:22; Eze 20:14
Deut. 32:27Eks 32:12; Nu 14:15, 16
Deut. 32:27Sl 115:2
Deut. 32:28Mt 13:15
Deut. 32:29Sl 81:13
Deut. 32:29Ho 14:9
Deut. 32:29Yer 2:19
Deut. 32:302Mb 24:24
Deut. 32:30Owe 2:14; 1Sa 12:9
Deut. 32:311Sa 2:2
Deut. 32:31Eks 14:25; 1Sa 4:8; Eza 1:2, 3
Deut. 32:32Yuda 7
Deut. 32:32Yes 5:4; Yer 2:21
Deut. 32:34Aro 2:5
Deut. 32:35Nah 1:2; Aro 12:19; Ahe 10:30
Deut. 32:35Sl 73:12, 18
Deut. 32:36Ahe 10:30
Deut. 32:36Owe 2:18; Sl 90:13; 106:45; 135:14
Deut. 32:37Owe 10:14
Deut. 32:38Ho 2:8; 1Ak 10:20, 21
Deut. 32:39Yes 41:4; 48:12
Deut. 32:39De 4:35
Deut. 32:391Sa 2:6; Sl 68:20
Deut. 32:392Mb 21:16, 18
Deut. 32:39Nu 12:13; Yer 17:14
Deut. 32:39Yes 43:13
Deut. 32:401Ti 1:17; Chv 10:5, 6
Deut. 32:41Nah 1:3
Deut. 32:41Yes 1:24; 59:18
Deut. 32:43Ge 12:2, 3; 1Mf 8:43; Aro 3:29; 15:10
Deut. 32:432Mf 9:7; Chv 6:10
Deut. 32:43Mik 5:15
Deut. 32:44Chv 15:3
Deut. 32:44Nu 11:28; De 31:22, 23
Deut. 32:46De 11:18
Deut. 32:46De 6:6, 7
Deut. 32:47Le 18:5; De 30:19; Aro 10:5
Deut. 32:49Nu 27:12
Deut. 32:49De 34:1
Deut. 32:49Ge 10:19; 15:18; Yos 1:3
Deut. 32:50Nu 20:28; 33:38
Deut. 32:51Nu 20:12, 13
Deut. 32:51Le 22:32; Yes 8:13
Deut. 32:52Nu 27:13, 14; De 3:27; 34:4, 5
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
  • 38
  • 39
  • 40
  • 41
  • 42
  • 43
  • 44
  • 45
  • 46
  • 47
  • 48
  • 49
  • 50
  • 51
  • 52
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 32:1-52

Deuteronomo

32 “Tamverani kumwamba inu, ndipo ine ndilankhula,

Dziko lapansi limve mawu a pakamwa panga.

 2 Malangizo anga adzagwa ngati mvula,

Mawu anga adzatsika ngati mame,

Ngati mvula yowaza pa udzu,

Ngatinso mvula yamphamvu pazomera.

 3 Chifukwa ndidzalengeza dzina la Yehova.+

Anthu inu, lengezani za ukulu wa Mulungu wathu!+

 4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+

Njira zake zonse ndi zolungama.+

Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita zinthu zopanda chilungamo.+

Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+

 5 Iwo ndi amene achita zinthu zoipa.+

Iwo si ana ake, ali ndi vuto ndi iwowo.+

Iwo ndi mʼbadwo wopotoka maganizo komanso wachinyengo!+

 6 Kodi Yehova mukuyenera kumuchitira zimenezi,+

Anthu opusa ndi opanda nzeru inu?+

Kodi iye si Atate wanu amene anakulengani,+

Amene anakupangani ndi kukukhazikitsani monga mtundu?

 7 Kumbukirani masiku akale,

Ganizirani zaka za mibadwo ya mʼmbuyo.

Funsani bambo anu ndipo akuuzani,+

Amuna achikulire pakati panu, ndipo akufotokozerani.

 8 Pamene Wamʼmwambamwamba anapereka cholowa ku mitundu ya anthu,+

Pamene analekanitsa ana a Adamu,*+

Anaika malire a anthu ena onse+

Poganizira chiwerengero cha ana a Isiraeli.+

 9 Pakuti anthu a Yehova ndi gawo lake.+

Yakobo ndiye cholowa chake.+

10 Anamupeza mʼdziko lachipululu,+

Mʼchipululu chopanda kanthu, molira zilombo.+

Anamuzungulira kuti amuteteze, anamusamalira,+

Ndipo anamuteteza ngati mwana wa diso lake.+

11 Monga mmene chiwombankhanga chimagwedezera chisa chake,

Mmene chimaulukira pamwamba pa ana ake,

Mmene chimatambasulira mapiko ake, kuti chitenge anawo,

Nʼkuwanyamula pamapiko ake,+

12 Ndi Yehova yekha amene anapitiriza kumutsogolera,*+

Panalibe mulungu wachilendo amene anali naye.+

13 Anamuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+

Moti anadya zokolola za mʼmunda.+

Anamudyetsa uchi wochokera mʼthanthwe,

Ndi mafuta ochokera mʼmwala wa nsangalabwi.

14 Anamudyetsanso mafuta a mkaka wa ngʼombe ndi mkaka wa nkhosa,

Pamodzi ndi nkhosa zabwino kwambiri,*

Komanso nkhosa zamphongo za ku Basana ndi mbuzi zamphongo,

Pamodzi ndi tirigu wabwino koposa.*+

Ndipo munamwa vinyo wochokera mʼmagazi a mphesa.*

15 Yesuruni* atanenepa, anapandukira mbuye wake.

Iwe wanenepa, wakula thupi, wakhuta mopitirira muyezo.+

Choncho iye anasiya Mulungu amene anamupanga,+

Ndipo ananyoza Thanthwe la chipulumutso chake.

16 Anamukwiyitsa ndi milungu yachilendo.+

Ankamukhumudwitsa ndi zinthu zonyansa.+

17 Iwo ankapereka nsembe kwa ziwanda, osati kwa Mulungu.+

Anapereka nsembe kwa milungu imene sankaidziwa,

Kwa milungu yatsopano yongobwera kumene,

Komanso kwa milungu imene makolo anu sankaidziwa.

18 Munaiwala Thanthwe+ limene linakuberekani,

Ndipo simunakumbukire Mulungu amene anakuberekani.+

19 Yehova ataona zimenezi anawakana+

Chifukwa chakuti ana ake aamuna ndi aakazi anamukhumudwitsa.

20 Choncho iye anati, ‘Ndiwabisira nkhope yanga,+

Ndione kuti ziwathera bwanji.

Chifukwa iwo ndi mʼbadwo wokonda zoipa,+

Ana osakhulupirika.+

21 Iwo andikwiyitsa* ndi milungu yabodza.+

Andikhumudwitsa ndi mafano awo opanda pake.+

Choncho ine ndiwachititsa nsanje ndi anthu opanda pake,+

Ndiwakhumudwitsa ndi mtundu wopusa.+

22 Mkwiyo wanga wayatsa moto+

Umene udzayaka mpaka kukafika pansi penipeni pa Manda,*+

Ndipo udzapsereza dziko lapansi ndi zokolola zake,

Komanso udzayatsa maziko a mapiri.

23 Ndidzawonjezera masoka awo,

Mivi yanga yonse ndidzaigwiritsa ntchito pa iwo.

24 Adzalefuka ndi njala+

Ndipo adzavutika ndi kutentha thupi koopsa komanso adzawonongedwa nʼkutheratu.+

Ndidzawatumizira zilombo za mano ataliatali+

Komanso njoka zapoizoni za mʼfumbi.

25 Kunja, lupanga lidzawasandutsa anamfedwa.+

Mʼnyumba, anthu adzagwidwa ndi mantha+

Zimenezi zidzachitikira mnyamata, namwali,

Mwana wamngʼono ndi munthu wa imvi.+

26 Ndikanatha kunena kuti: “Ndidzawabalalitsa,

Ndidzachititsa kuti anthu asakumbukirenso za iwo,”

27 Koma ndinkaopa zimene mdani anganene,+

Chifukwa adaniwo angaganize molakwika.+

Iwo anganene kuti: “Tapambana chifukwa cha mphamvu zathu,+

Si Yehova amene wachita zonsezi.”

28 Chifukwa iwo ndi mtundu wopanda nzeru,*

Ndipo ndi osazindikira.+

29 Zikanakhala bwino ngati akanakhala anzeru,+ chifukwa akanaganizira mozama zimenezi.+

Akanaganizira kuti ziwathera bwanji.+

30 Kodi munthu mmodzi angathamangitse bwanji anthu 1,000,

Kapena anthu awiri angathamangitse bwanji anthu 10,000?+

Nʼzosatheka, pokhapokha Thanthwe lawo litawagulitsa,+

Komanso ngati Yehova atawapereka.

31 Chifukwa thanthwe lawo si lofanana ndi Thanthwe lathu,+

Ndipo adani athu akudziwa bwino zimenezi.+

32 Mtengo wawo wa mpesa ndi wochokera ku mtengo wa mpesa wa ku Sodomu,

Ndi kuminda ya mʼmapiri a ku Gomora.+

Zipatso zawo za mphesa ndi zapoizoni

Ndipo ndi zowawa.+

33 Vinyo wawo ndi poizoni wa njoka,

Ndi poizoni woopsa wa mamba.

34 Kodi ine sindinasunge zimenezi,

Nʼkuziikira chidindo mʼnyumba yanga yosungira zinthu?+

35 Kubwezera ndi kwanga, chilangonso ndi changa.+

Zimenezi zidzachitika pa nthawi yoikidwiratu phazi lawo likadzaterereka,+

Chifukwa tsiku la tsoka lawo layandikira,

Ndipo zowagwera zifika mofulumira.’

36 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake,+

Ndipo adzamvera chisoni atumiki ake+

Akadzaona kuti mphamvu zawo zatha,

Komanso kuti kwangotsala anthu ovutika ndi ofooka.

37 Ndiyeno iye adzanena kuti, ‘Ili kuti milungu yawo,+

Thanthwe limene anathawirako,

38 Milungu imene inkadya mafuta a nsembe zawo,*

Ndi kumwa vinyo wa nsembe zawo zachakumwa?+

Ibwere kudzakuthandizani.

Ikhale malo anu othawirako.

39 Onani tsopano kuti ndine Mulungu,+

Ndipo palibe Mulungu wina koma ine ndekha.+

Ndimapha komanso ndimapereka moyo.+

Ndimavulaza,+ ndipo ndidzachiritsa,+

Palibe aliyense amene angapulumutse munthu mʼdzanja langa.+

40 Ndakweza dzanja langa kumwamba

Ndipo ndikulumbira kuti: “Ine, Mulungu wamuyaya, ndikulumbira pa dzina langa,”+

41 Ndikanola lupanga langa lonyezimira,

Nʼkukonzekeretsa dzanja langa kuti lipereke chiweruzo,+

Ndidzabwezera adani anga,+

Ndipo ndidzapereka chilango kwa amene amadana nane.

42 Ndidzaledzeretsa mivi yanga ndi magazi,

Ndipo lupanga langa lidzadya nyama,

Ndi magazi a anthu ophedwa komanso ogwidwa,

Ndiponso mitu ya atsogoleri a adani.’

43 Inu anthu a mitundu ina, sangalalani limodzi ndi anthu ake,+

Chifukwa adzabwezera magazi a atumiki ake,+

Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+

Komanso adzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”*

44 Ndiyeno Mose anabwera nʼkulankhula mawu onse a nyimbo iyi anthu onse akumva,+ iye pamodzi ndi Hoshiya*+ mwana wa Nuni. 45 Mose atamaliza kulankhula mawu onsewa kwa Aisiraeli onse, 46 anawauza kuti: “Ganizirani mofatsa mawu onse okuchenjezani amene ndikulankhula nanu lero,+ kuti muuze ana anu kuti azionetsetsa kuti akuchita zimene mawu onse a Chilamulo ichi akunena.+ 47 Chifukwa amenewa si mawu opanda pake kwa inu, koma angakuthandizeni kukhala ndi moyo.+ Mukamatsatira mawu amenewa mudzakhala ndi moyo wautali mʼdziko limene mukuwoloka Yorodano kuti mukalitenge kukhala lanu.”

48 Yehova analankhula ndi Mose pa tsiku lomweli kuti: 49 “Kwera mʼphiri ili la Abarimu,+ phiri la Nebo,+ limene lili mʼdziko la Mowabu, moyangʼanizana ndi Yeriko, ndipo uone dziko la Kanani limene ndikupereka kwa Aisiraeli kuti likhale lawo.+ 50 Kenako ukafera paphiri limene ukufuna kukwerali nʼkuikidwa mʼmanda ngati mmene anachitira ndi makolo ako,* mofanana ndi Aroni mʼbale wako amene anafera paphiri la Hora+ nʼkuikidwa mʼmanda ngati mmene anachitira ndi makolo ake. 51 Izi zili choncho chifukwa awirinu simunakhale okhulupirika kwa ine pakati pa Aisiraeli kumadzi a pa Meriba+ ku Kadesi, mʼchipululu cha Zini, chifukwa simunandilemekeze pamaso pa Aisiraeli.+ 52 Iwe udzaona dzikolo uli patali, koma sudzalowa mʼdziko limene ndikupereka kwa Aisiraeli.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena