Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nyimbo ya Solomo 7
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Zimene Zili Mʼbuku la Nyimbo ya Solomo

    • MSULAMI ALI KU YERUSALEMU (3:6–8:4)

Nyimbo ya Solomo 7:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 4:5

Nyimbo ya Solomo 7:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 1:10
  • +Nym 4:4
  • +Nym 4:1
  • +Nu 21:25; Yos 21:8, 39

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/2006, tsa. 20

    11/15/1987, tsa. 25

Nyimbo ya Solomo 7:5

Mawu a M'munsi

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “yatengeka.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 35:2
  • +Nym 6:5
  • +Est 8:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/1996, tsa. 7

Nyimbo ya Solomo 7:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 7:3; 8:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/15/2007, tsa. 32

Nyimbo ya Solomo 7:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 2:16; 6:3

Nyimbo ya Solomo 7:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 1:14

Nyimbo ya Solomo 7:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 2:13
  • +Nym 6:11
  • +Nym 1:2; 4:10

Nyimbo ya Solomo 7:13

Mawu a M'munsi

  • *

    “Mandereki” ndi chitsamba cha mʼgulu la mbatata, chimene chimabereka zipatso.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 30:14
  • +Nym 4:16

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Nyimbo 7:3Nym 4:5
Nyimbo 7:4Nym 1:10
Nyimbo 7:4Nym 4:4
Nyimbo 7:4Nym 4:1
Nyimbo 7:4Nu 21:25; Yos 21:8, 39
Nyimbo 7:5Yes 35:2
Nyimbo 7:5Nym 6:5
Nyimbo 7:5Est 8:15
Nyimbo 7:7Nym 7:3; 8:10
Nyimbo 7:10Nym 2:16; 6:3
Nyimbo 7:11Nym 1:14
Nyimbo 7:12Nym 1:2; 4:10
Nyimbo 7:12Nym 2:13
Nyimbo 7:12Nym 6:11
Nyimbo 7:13Ge 30:14
Nyimbo 7:13Nym 4:16
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Nyimbo ya Solomo 7:1-13

Nyimbo ya Solomo

7 “Mapazi ako akukongola kwambiri munsapato zako,

Iwe mwana wamkazi wolemekezeka.

Ntchafu zako nʼzoumbidwa bwino ngati zinthu zodzikongoletsera,

Ntchito ya manja a munthu waluso.

 2 Mchombo wako uli ngati mbale yolowa.

Vinyo wosakaniza bwino asasowepo.

Mimba yako ili ngati mulu wa tirigu,

Wozunguliridwa ndi maluwa.

 3 Mabere ako awiri ali ngati ana awiri a insa,

Ana amapasa a insa.+

 4 Khosi lako+ lili ngati nsanja ya mnyanga wa njovu.+

Maso ako+ ali ngati madamu a madzi a ku Hesiboni,+

Amene ali pafupi ndi geti la Bati-rabimu.

Mphuno yako ili ngati nsanja ya ku Lebanoni,

Imene inayangʼana cha ku Damasiko.

 5 Mutu wako ndi wokongola ngati phiri la Karimeli,+

Ndipo tsitsi lako lopotanapotana+ lili ngati ubweya wa nkhosa wapepo.+

Mfumu yakopeka* ndi tsitsi lako lalitali lokongolalo.

 6 Ndiwe wokongola kwambiri mtsikana iwe ndipo ndiwe wosangalatsa,

Kuposa zinthu zina zonse zimene zimasangalatsa mtima wa munthu.

 7 Ndiwe wamtali ngati mtengo wa kanjedza,

Ndipo mabere ako ali ngati zipatso zake.+

 8 Ine ndinanena kuti, ‘Ndikwera mtengo wa kanjedza

Kuti ndikathyole nthambi zake zokhala ndi zipatso.’

Mabere ako akhale ngati phava la zipatso za mpesa,

Ndipo mpweya wamʼkamwa mwako ununkhire ngati maapozi,

 9 Ndipo mʼkamwa mwako mununkhire ngati vinyo wabwino kwambiri.”

“Adutse mwamyaa kukhosi kwa wokondedwa wanga,

Ngati vinyo amene amadutsa mwamyaa pakamwa nʼkuyambitsa tulo kwa amuna.

10 Wachikondi wangayo, ine ndine wakewake,+

Ndipo iye amalakalaka ineyo.

11 Bwera wachikondi wanga,

Tiye tipite kumunda.

Tiye tikakhale pakati pa maluwa a hena.+

12 Tiye tilawirire mʼmamawa tipite kuminda ya mpesa.

Tikaone ngati mitengo ya mpesa yaphukira,

Ngati maluwa amasula+

Ngati mitengo ya makangaza yachita maluwa.+

Kumeneko ndikakusonyeza chikondi changa.+

13 Zipatso za mandereki*+ zikununkhira,

Pamakomo olowera kunyumba zathu pali zipatso zosiyanasiyana zokoma kwambiri.+

Ndakusungira zipatso zatsopano ndi zakale zomwe,

Iwe wachikondi wanga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena