Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 41:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova adzamuteteza ndi kumusunga ali wamoyo.+

      Adzatchedwa wodala padziko lapansi.+

      Ndipo Mulungu sangamupereke kwa adani ake.+

  • Miyambo 11:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Munthu woipa amapeza malipiro achinyengo,+ koma wofesa chilungamo amapeza malipiro enieni.+

  • Miyambo 19:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Wokomera mtima munthu wonyozeka akukongoza Yehova,+ ndipo adzam’bwezera zimene anachitazo.+

  • Mlaliki 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngakhale woipa atachita zoipa+ maulendo 100 n’kukhala ndi moyo wautali akuchitabe zofuna zake, ine ndikudziwa kuti anthu amene amaopa Mulungu woona zidzawayendera bwino,+ chifukwa chakuti anali kumuopa.+

  • Yesaya 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Amuna inu, nenani kuti anthu olungama zidzawayendera bwino,+ chifukwa adzadya zipatso za zochita zawo.+

  • Luka 1:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Chifundo chake chakhala pa amene amamuopa ku mibadwomibadwo.+

  • Aheberi 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti Mulungu si wosalungama woti angaiwale ntchito yanu ndi chikondi chimene munachisonyeza pa dzina lake,+ mwa kutumikira oyera+ ndipo mukupitiriza kuwatumikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena