Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Uzimvera Yehova Mulungu wako mwa kuyenda m’njira zake,+ kusunga malamulo ake, zigamulo zake,+ ndi maumboni* ake, malinga ndi zimene zinalembedwa m’chilamulo cha Mose.+ Uzitero kuti udzakhale wanzeru m’zochita zako zonse, ndiponso kulikonse kumene udzapite.

  • Salimo 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chilamulo+ cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa moyo.+

      Zikumbutso+ za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+

  • Salimo 107:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Wanzeru ndani? Iye aona zimenezi,+

      Ndi kuchita chidwi ndi ntchito za Yehova zosonyeza kukoma mtima kwake kosatha.+

  • Salimo 111:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chiyambi cha nzeru ndicho kuopa Yehova.+

      ש [Sin]

      Onse otsatira malamulo a Mulungu ndi ozindikira.+

      ת [Taw]

      Iye ayenera kutamandidwa mpaka muyaya.+

  • Salimo 119:98
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  98 Malamulo anu amandichititsa kukhala wanzeru kuposa adani anga,+

      Chifukwa ndi anga mpaka kalekale.+

  • Miyambo 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Munthu wanzeru mumtima mwake amamvera malamulo,+ koma wamilomo yopusa amaponderezedwa.+

  • Yeremiya 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Anthu anzeru achita manyazi.+ Achita mantha ndipo adzagwidwa. Taonani! Iwo akana mawu a Yehova. Kodi ali ndi nzeru yotani tsopano?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena