15 Mfumu Solomo inaitana anthu ogwira ntchito yokakamiza+ kuti adzamange nyumba ya Yehova,+ nyumba yake, Chimulu cha Dothi,*+ khoma+ lozungulira Yerusalemu, ndiponso mizinda ya Hazori,+ Megido,+ ndi Gezeri.+
67 Chotero anawapatsa mzinda wothawirako wa Sekemu+ ndi malo ake odyetserako ziweto m’dera lamapiri la Efuraimu, mzinda wa Gezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto,