Yoswa 12:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Mfumu ya Egiloni,+ imodzi. Mfumu ya Gezeri,+ imodzi. Yoswa 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Aefuraimu analephera kupitikitsa Akanani+ amene anali kukhala ku Gezeri.+ Choncho Akananiwo akukhalabe pakati pa Aefuraimu mpaka lero,+ ndipo anayamba kuwagwiritsa ntchito yaukapolo.+ Yoswa 21:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Motero anawapatsa mzinda wothawirako+ munthu amene wapha mnzake,+ wa Sekemu,+ ndi malo ake odyetserako ziweto+ m’dera lamapiri la Efuraimu. Anawapatsanso Gezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Oweruza 1:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Fuko la Efuraimu nalonso silinapitikitse Akanani amene anali kukhala ku Gezeri, moti Akananiwo anakhalabe pakati pawo ku Gezeriko.+ 1 Mafumu 9:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 (M’mbuyomo, Farao mfumu ya Iguputo inabwera n’kulanda mzinda wa Gezeri n’kuutentha ndi moto. Akanani+ okhala mumzindawo inawapha. Kenako inaupereka kwa mwana wake wamkazi+ monga mphatso pamene anali kukwatiwa ndi Solomo.)
12 Mfumu ya Egiloni,+ imodzi. Mfumu ya Gezeri,+ imodzi. Yoswa 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Aefuraimu analephera kupitikitsa Akanani+ amene anali kukhala ku Gezeri.+ Choncho Akananiwo akukhalabe pakati pa Aefuraimu mpaka lero,+ ndipo anayamba kuwagwiritsa ntchito yaukapolo.+ Yoswa 21:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Motero anawapatsa mzinda wothawirako+ munthu amene wapha mnzake,+ wa Sekemu,+ ndi malo ake odyetserako ziweto+ m’dera lamapiri la Efuraimu. Anawapatsanso Gezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Oweruza 1:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Fuko la Efuraimu nalonso silinapitikitse Akanani amene anali kukhala ku Gezeri, moti Akananiwo anakhalabe pakati pawo ku Gezeriko.+ 1 Mafumu 9:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 (M’mbuyomo, Farao mfumu ya Iguputo inabwera n’kulanda mzinda wa Gezeri n’kuutentha ndi moto. Akanani+ okhala mumzindawo inawapha. Kenako inaupereka kwa mwana wake wamkazi+ monga mphatso pamene anali kukwatiwa ndi Solomo.)
10 Aefuraimu analephera kupitikitsa Akanani+ amene anali kukhala ku Gezeri.+ Choncho Akananiwo akukhalabe pakati pa Aefuraimu mpaka lero,+ ndipo anayamba kuwagwiritsa ntchito yaukapolo.+
21 Motero anawapatsa mzinda wothawirako+ munthu amene wapha mnzake,+ wa Sekemu,+ ndi malo ake odyetserako ziweto+ m’dera lamapiri la Efuraimu. Anawapatsanso Gezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto,
29 Fuko la Efuraimu nalonso silinapitikitse Akanani amene anali kukhala ku Gezeri, moti Akananiwo anakhalabe pakati pawo ku Gezeriko.+
16 (M’mbuyomo, Farao mfumu ya Iguputo inabwera n’kulanda mzinda wa Gezeri n’kuutentha ndi moto. Akanani+ okhala mumzindawo inawapha. Kenako inaupereka kwa mwana wake wamkazi+ monga mphatso pamene anali kukwatiwa ndi Solomo.)